Onani zimene zilipo

Zokhudza Mboni za Yehova

Mumationa tikugwila nchito yathu yolalikila. Mwina munaŵelengapo za ife pa nyuzi, kapena munamvapo ena akamba za ife. Koma kodi mumazidziŵa bwino motani Mboni za Yehova?

Onaninso: Kodi Mboni za Yehova zimakhulupilila zotani?

Zimene Timakhulupilila na Nchito Zathu

Mafunso Amene Amafunsidwa Kawili-kaŵili Ponena za Mboni za Yehova

Dziŵani mayankho pa mafunso amene mungakhale nawo ponena za ife.

Zimene Mboni za Yehova Zimacita

Ticokela m’maiko oposa 230 komanso mikhalidwe yosiyanasiyana. Mwina mumaidziŵa bwino nchito yathu yolalikila, koma timathandizanso anthu a m’dela lathu m’njiila zina.

Kuphunzila Baibo Kwaulele

N’cifukwa Ciani Muyenela Kuphunzila Baibulo?

Anthu mamiliyoni akupedza mayankho a mafunso awo ofunika kwambili m’Baibo. Kodi mungafune kukhala m’modzi wa iwo?

Kodi Phunzilo la Baibulo Limacitika Bwanji?

Zungulile dziko lonse, Mboni za Yehova zimadziŵika cifukwa ca pulogilamu yawo yophunzitsa Baibo kwaulele. Onani mmene imacitikila.

Pemphani kuti wa Mboni adzakucezeleni

Kambilanani nkhani ya m’Baibo na Mboni za Yehova, kapena laŵani maphunzilo a Baibo amene timapeleka.

Misonkhano na Zocitika

N’ciani Cimacitika ku Nyumba ya Ufumu?

Tambani vidiyo kuti muone zimene zimacitika.

Kapezekemponi pa Misonkhano ya Mboni za Yehova

Fufuzani kumene timakumana komanso mmene timalambilila. Onse ni olandilidwa ndipo sipakhala kuyendetsa mbale ya zopeleka.

Cikumbutso ca Imfa ya Yesu

Caka ciliconse anthu mamiliyoni ambili amasonkhana pamodzi kuti acite mwambo wokumbukila imfa ya Yesu. Bwelani mudzamve mmene cocitika cofunika kwambili cimeneci cimakukhudzilani.

Maofesi Anthambi

Dziŵitsani Mboni za Yehova

Maadilesi ndi manambala a foni a maofesi athu a pa dziko lonse.

Kukaona Malo pa Beteli

Fufuzani kumene mungayende kukaona malo pa Beteli kufupi na kwanu.

Kodi Ndalama Zoyendetsela Nchito ya Mboni za Yehova Zimacokela Kuti?

Ŵelengani kuti mudziŵe cifukwa cake nchito yolalikila padziko lonse ikupita patsogolo kwambili ngakhale kuti sitiyendetsa mbale ya zopeleka ndi kupeleka cakhumi.

Ndani Amene Akucita Cifunilo ca Yehova Masiku Ano?

Mboni za Yehova zimapezeka padziko lonse, ndipo zimacokela m’mafuko ndi zikhalidwe zosiyana-siyana. Kodi zatheka bwanji kuti anthu osiyana-siyana conco agwilizane capamodzi?