Mfundo Zachidule—Croatia
- 4,038,000—Chiwerengero cha anthu
- 4,687—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
- 57—Mipingo
- Pa anthu 870 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi
NKHANI
A Mboni Anachita Nawo Chionetsero cha Mabuku Pamwambo Wodziwika Kwambiri ku Croatia
A Mboni za Yehova anachita nawo chionetsero chamabuku ku Croatia. Mwambowu unachitika pa 11 mpaka pa 16 November 2014 ndipo unali wa nambala 37. Anthu a m’mayiko osiyanasiyana anapita kukaonetsa mabuku awo.