Mfundo Zachidule—Ireland
- 7,052,000—Chiwerengero cha anthu
- 7,974—Chiwerengero cha Mboni za Yehova
- 121—Mipingo
- Pa anthu 907 alionse pali wa Mboni za Yehova m’modzi
NTCHITO YOLALIKIRA
Kulalikira M’dera Lakutali M’dziko la Ireland
Banja likufotokoza mmene ntchito yolalikira ku Ireland, yawathandizira kukhala ogwirizana.
ZOCHITIKA ZAPADERA
Msonkhano Wapadera ku Ireland
A Mboni za Yehova ku Dublin m’dziko la Ireland, analandira alendo ochokera m’mayiko ena amene anabwera ku Msonkhano Wapadera wa mu 2012, umene unali ndi mutu wakuti ‘Tetezani Mtima Wanu!’ Onani zimene ena ananena zokhudza msonkhano umenewu.