Pitani ku nkhani yake

BAIBULO LIMASINTHA ANTHU

Ndinkafunitsitsa Kuthana ndi Kupanda Chilungamo

Ndinkafunitsitsa Kuthana ndi Kupanda Chilungamo

Rafika analowa m’gulu la anthu ofuna kuthana ndi zinthu zopanda chilungamo. Koma anaona kuti m’Baibulo muli lonjezo loti ndi Ufumu wa Mulungu wokha womwe udzabweretse mtendere komanso chilungamo padzikoli.