BAIBULO LIMASINTHA ANTHU
Ndinkafunitsitsa Kuthana ndi Kupanda Chilungamo
Rafika analowa m’gulu la anthu ofuna kuthana ndi zinthu zopanda chilungamo. Koma anaona kuti m’Baibulo muli lonjezo loti ndi Ufumu wa Mulungu wokha womwe udzabweretse mtendere komanso chilungamo padzikoli.