Pitani ku nkhani yake

Phunziro 8: Uzikhala Waukhondo

Phunziro 8: Uzikhala Waukhondo

Kodi inuyo mukhoza kukhala aukhondo komanso oyera ngati Yehova? Kalebe anatengera chitsanzo cha Yehova pa nkhani imeneyi.

Mwina Mungakondenso Kudziwa Izi

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Thandizani Kalebe Kukonza M’nyumba

Pangani dawunilodi kapena sindikizani tsambali ndipo muthandizeni Kalebe kupeza zidole zake 5 zomwe akufunika kuchotsa m’nyumba.

ZOCHITA PA GAWO LA KHALANI BWENZI LA YEHOVA

Timapepala Tazithunzi Tofunika Kusunga!

Mungagwiritsire ntchito timapepalati kudziwa malo omwe mumawerenga m’mabuku anu!

MAVIDIYO

Phunzirani kwa Anzake a Yehova

Phunzirani zambiri kuchokera kwa anthu otchulidwa m’Baibulo omwe anakhala mabwenzi a Yehova!

ZIMENE BAIBULO LIMAPHUNZITSA

Zoti Ana Achite

Gwiritsani ntchito zinthu zosangalatsa zimenezi, nkhani zochokera m’Baibulo komanso makadi a anthu otchulidwa m’Baibulo pophunzitsa ana mfundo za m’Baibulo.