Pitani ku nkhani yake

Kukhulupirira Kwambiri Mulungu

Why Believe in God?

Kodi Mulungu Alipodi?

Baibulo limayankha mogwira mtima mafunso 5 ofunika kwambiri.

Kudziwa Bwino Mulungu

Kodi Dzina la Mulungu Ndi Ndani?

Kodi mumadziwa kuti Mulungu ali ndi dzina limene limamusiyanitsa ndi milungu ina?

Kodi N’chiyani Chingakuthandizeni Kudziwa Bwino Mulungu?

Zinthu 7 zimene zingathandize kuti mukhale pa ubwenzi wabwino ndi Mulungu.

Timaphunzira za Mulungu Kuchokera kwa Aneneri Ake

Aneneri okhulupirika atatu amatithandiza kuphunzira za Mulungu komanso zimene tingachite kuti tidzalandire madalitso.

Kodi Mulungu Ndi Wosamvetsetseka?

Zinthu zina zimene n’zovuta kumvetsa ponena za Mulungu zimatithandiza kuti timuyandikire.

Kodi N’zotheka Kuona Mulungu Yemwe ndi Wosaoneka?

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe mmene mungagwiritsire ntchito “maso a mtima wanu” kuona Mulungu.

Choonadi Chonena za Mulungu Komanso Khristu

Kodi Yehova Mulungu ndi Yesu Khristu ndi osiyana bwanji?

Kodi Mulungu Ali Ndi Makhalidwe Otani?

Kodi makhalidwe aakulu a Mulungu ndi ati?

Kodi Mulungu Amachita Chidwi ndi Zimene Zimakuchitikirani?

Kodi n’chiyani chikusonyeza kuti Mulungu amachita chidwi ndi zimene zimachitika pa moyo wathu?

Kodi Mulungu Amadziwa Mmene Mumamvera?

Baibulo limatitsimikizira kuti Mulungu amachita nafe chidwi, amatimvetsa komanso amadziwa mmene timamvera.

The Value of Faith

N’chifukwa Chiyani Timafunikira Mulungu?

Werengani kuti mudziwe mmene kukhala pa ubwenzi ndi Mulungu kungatithandizire kuti tikhale ndi moyo wosangalala.

Kodi Baibulo Limanena Zotani Zokhudza Chikhulupiriro?

Baibulo limanena kuti ‘popanda chikhulupiriro n’zosatheka kukondweretsa Mulungu.’ Chikhulupiliro n’chiyani? Mungatani kuti mukhale ndi chikhulupiriro?

Baibulo Linandithandiza Kupeza Mayankho a Mafunso Anga

Mayli Gündel anasiya kukhulupirira zoti kuli Mulungu bambo ake atamwalira. N’chiyani chinamuthandiza kuyambanso kukhulupirira zoti kuli Mulungu komanso kukhala ndi mtendere wamumtima?

Ndinasiya Kupita Kuchipembedzo Chilichonse

Tom ankafunitsitsa kuti azikhulupirira Mulungu koma anakhumudwa ndi zochita komanso miyambo yachabechabe ya chipembedzo. Kodi kuphunzira Baibulo kunamuthandiza bwanji kuti akhale ndi chiyembekezo?

Challenges to Faith

Kodi Tingathetse Bwanji Chidani?​—Mulungu Angakuthandizeni Kuthetsa Mtima Wachidani

Mzimu woyera wa Mulungu ungakuthandizeni kukhala ndi makhalidwe amene angakuthandizeni kuthetsa chidani.

Kodi Chipembedzo Chasanduka Bizinezi Yotentha?

Nthawi zina anthu amene amabwera kutchalitchi ndi osauka, pomwe m’busa wa tchalitchicho ndi wolemera kwambiri.

N’chifukwa Chiyani Mulungu Amalola Kuti Anthu Azivutika?

Anthu ambiri amafuna kudziwa kuti n’chifukwa chiyani padzikoli pali mavuto ambiri. Baibulo limapereka yankho logwira mtima pa nkhaniyi.

N’chifukwa Chiyani Ena Amati Mulungu Ndi Wankhanza?

Anthu ambiri amaona kuti Mulungu ndi wankhanza kapena alibe chidwi ndi anthu. Kodi Baibulo limati chiyani pa nkhaniyi?

Drawing Close to God

Kodi N’zotheka Mulungu Kukhala Mnzanu Wapamtima?

Pali anthu enanso ambiri amene amaona kuti Mulungu ndi mnzawo wapamtima.

Kodi Mungatani Kuti Muyandikire Mulungu?

Werengani nkhaniyi kuti mudziwe ngati Mulungu amamvetsera mapemphero onse, mmene tiyenera kupempherera, komanso zinthu zina zimene tingachite kuti tiyandikire Mulungu.

N’chifukwa Chiyani Mphatso Imene Mulungu Watipatsa Ndi Yamtengo Wapatali?

Kodi ndi zinthu ziti zimene zimachititsa kuti mphatso ikhale yamtengo wapatali? Kuganizira zimenezi kungatithandize kuti tiziyamikira kwambiri dipo.

Tizikhulupirira Zimene Baibulo Limanena pa Nkhani ya Zoyenera Ndi Zosayenera

Kodi mungatsimikizire bwanji kuti Baibulo lili ndi malangizo othandiza kusankha zoyenera pa nkhani ya makhalidwe abwino?

Kodi Anthufe Tingasangalatsedi Mulungu?

Tingapeze yankho tikaganizira zimene zinachitikira Yobu, Loti, ndi Davide, omwe analakwitsapo zinthu zazikulu.

Kodi Zingatheke Bwanji Kuti Mudzakhale ndi Moyo Wosatha?

Baibulo limalonjeza kuti anthu amene amachita zimene Mulungu amafuna akhoza kudzakhala ndi moyo wosatha. Onani zinthu zitatu zimene Mulungu amafuna kuti tizichita.

Kodi Kudziwa Zoti Mulungu Amatiganizira Kungatithandize Bwanji?

Malemba amatithandiza kuti tikhale ndi chikhulupiriro choti Mulungu adzakwaniritsa zimene watilonjeza.